Jump to
Sections of this page
Accessibility Help
Press alt + / to open this menu
We won’t support this browser soon. For a better experience, we recommend using another browser. Learn More

Facebook

Forgot account?
Sign Up
See more of Malawi News Agency on Facebook
Log In
or
Create New Account
See more of Malawi News Agency on Facebook
Forgot account?
or
Create New Account
Not Now
Related Pages
  • United Nations
    Organization
  • POLITICS & ELECTIONS FORUM
    Political Organization
  • Breaking News in Malawi
    Media/News Company
  • NyasaTimes Newspaper
    News & Media Website
  • Zodiak Online
    Advertising/Marketing
  • Malawi Daily News Online
    Newspaper
  • Nation Publications Limited
    Media/News Company
  • NYASA TIMES Malawi - breaking news
    Sports
  • Malawi24
    Media/News Company
  • Citizen Online
    Media/News Company
  • Zodiak Broadcasting Station -ZBS TV
    TV Channel
  • MBC Malawi Ltd
    Music
Recent Post by Page
Malawi News Agency
Today at 2:33 AM
BREAKING NEWS: EU OBSERVER MISSION IKUZAPEMPHA MUNTHARIKA KUTI ATULU...SE PANSI UDINDO WAKE European Union observer mission yonse yomwe inalipo nthawi yachisankho yalengeza kuti ibwelanso ku dziko lino mawa kuzakhala pansi ndi mtsogoleri wa dziko lino Peter Muntharika ndinso kumupempha kuti atule pansi udindo wake mwawulemu ngati Court litamupeza kuti iye ndi olakwa. Malingana ndima report omwe atipeza kuchokela ku EU, bungweli lamvesedwa kuti masankho sanayende bwino ndipo akuyenela kuchitikanso. Pofuna kulimbikisa ufulu ndi malamulo a dziko lino, bungwe la EU laganiza zokambilana ndi Peter Muntharika kuti atule pansi udindo wake mwaulemu ndinso kuzapempha a Malawi kuti azavomeleze chigamulo cha court See More
Malawi News Agency
Today at 2:13 AM
TB JOSHUA WATI U VICE PRESIDENT WA CHILIMA SUNATHE (segulani ma pict...ures pa number kuti muone) TB Joshua anapempha anthu omwe amapemphela nawo mu tchalitchi mwake kuti amuthandize kupemphelela Vice President modzi wakale muno mu Africa ati ponena kuti u Vice President wake sunathe ndinso akumana ndi mikwingwilima pogwila ntchito yake. Monga mukuonela pa number 6 ndimene TB Joshua walembela pa Facebook page yake. Ulosiwu ukulunjika kwa Dr Saulos Chilima yemwe ali Vice President wakale mdziko lino ndinso ndiyekhayo yemwe ali ndi mulandu okhuza zisankho muno mu Africa. Pali unthenga wina waboza omwe Nyasatimes ikufalisa onena kuti TB Joshua wanena kuti "NO CHANGE FOR MALAWI" ife a Malawi News Agency chinatikomela ntima kuyimbila phone mpingo wa TB Joshua kuti tipeze umboni weni weni pa nkhaniyi koma tapeza kuti unthengawu ngwaboza ndipo sukuyenela kumveledwa. Mukasegula page ya TB Joshua mupeza kuti TB Joshua sananene kalikonse kokhuza Malawi ndinso kuti sanalunjike mwachindunji pa nkhani yokhuza Vice President powopesa zipolowe bwalo lisanagamule. Joshua sanalunjike nkhani yokhuza vice President ku Malawi kamba amaziwa kuti zitha kuyambisa chipolowe munadela ambili maka pa nthawi ino yomwe asilikari sanakonzeke kuyamba ntchito yokhazikisa bata. Muunthenga wake TB Joshua wati iye apemphelela Vice President wakale wa dziko lino kamba azakhala ndi pressure yothana ndimavuto mu m'dziko lino pakanthawi kochepa kuti masankho achitike malingana ndima report omwe achokela ku mpingo wa TB Joshua See More
Malawi News Agency
Yesterday at 11:46 AM
AKULU AKULU A DPP APANGA UPO OFUNA KUPHA MBONI ZA MCP NDI UTM NDICHO...LINGA CHOTI AKAWINE MULANDU KU COURT LA SUPREME Kagulu ka akuluakulu ena a DPP monga Peter Muntharika, Charles Mchacha, Nicholas Dausi, Grezeeder Jeffrey, Chimunthu Banda, Ntompwa 1, Duncan Mwapasa ndinso bodyguard wa Peter Muntharika Norman Chisale apanga upo oti aphe mboni zikuzikulu za MCP ndi UTM pazolinga zoti akakasuma kubwalo la Supreme mbali zosusa zizalephele kukhala ndi mboni zokwanila. Izi zaziwika lero pomwe Nicholas Dausi ndi wamkulu wapolisi usiku uno anachitisa msonkhano ndi apolisi ena okwanila 40 ochokela ku mwela komwe mwazina amakambilana zoyamba kupha Daud Suleman kusilizila Ndasauka. Panthawi ino yomwe antolankhani athu apeza izi, mboni zina za DR Saulosi Chilima zikukumana ndimikwingwilima yochokela kwa apolisi ena omwe akumapita kumanyumba kwawongati mbava, mbonizi ndimonga Miriam Gwalidi ndi Darlington Ndasauka. Nawo a Daud Suleman omwe ndi mboni ya Dr Lazalous Chakwera akukumana ndi mavuto ochuluka kamba anthu a DPP akumapita ku nyumba kwake usiku ndimifuti. Pakanali pano apolisi angoti akufufuzabe. Norman Chisare ndi oophya kwambili ndipo amaziwa kuphedwe kamunthu mwachisilikari ndiyenso anapha Njaunju See More
 
  • English (US)
  • Español
  • Français (France)
  • 中文(简体)
  • العربية
  • Português (Brasil)
  • Italiano
  • 한국어
  • Deutsch
  • हिन्दी
  • 日本語
  • Sign Up
  • Log In
  • Messenger
  • Facebook Lite
  • Watch
  • People
  • Pages
  • Page Categories
  • Places
  • Games
  • Locations
  • Marketplace
  • Groups
  • Instagram
  • Local
  • Fundraisers
  • Services
  • About
  • Create Ad
  • Create Page
  • Developers
  • Careers
  • Privacy
  • Cookies
  • Ad Choices
  • Terms
  • Help
  • Settings
  • Activity Log
Facebook © 2020